4 Ndipo iwe ugonere pansi mbali yako ya kumanzere, nuikepo mphulupulu ya nyumba ya Israyeli; monga mwa kuwerenga kwa masiku amene udzagonapo udzasenza mphulupulu yao.
Werengani mutu wathunthu Ezekieli 4
Onani Ezekieli 4:4 nkhani