Ezekieli 4:6 BL92

6 Ndipo utatsiriza awa, ugonerenso mbali yako ya kumanja, ndi kusenza mphulupulu ya nyumba ya Yuda; ndakuikira masiku makumi anai, kuliyesa tsiku limodzi ngati caka cimodzi.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 4

Onani Ezekieli 4:6 nkhani