23 Ndipo panali cipata ca bwalo lam'kati, copenyana ndi cipata cinzace cakunja kumpoto, ndi ca kum'mawa; ndipo anayesa kuyambira kucipata kufikira kucipata mikono zana.
Werengani mutu wathunthu Ezekieli 40
Onani Ezekieli 40:23 nkhani