Ezekieli 42:20 BL92

20 Analiyesa mbali zace zinai, linali nalo linga pozungulira pace, utali wace mazana asanu, citando cace mazana asanu, kusiyanitsa pakati pa zopatulika ndi zawamba.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 42

Onani Ezekieli 42:20 nkhani