Ezekieli 44:19 BL92

19 Ndipo akaturukira ku bwalo lakunja, ku bwalo lakunja kuti anthu, azibvula zobvala zao zimene atumikira nazo, naziike m'zipinda zopatulika, nabvale zobvala zina; angapatule anthu ndi zovala zao.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 44

Onani Ezekieli 44:19 nkhani