Ezekieli 44:25 BL92

25 Ndipo asayandikire kwa munthu ali yense wakufa, angadzidetse; koma cifukwa ca atate, kapena mai, kapena mwana wamwamuna, kapena mwana wamkazi, kapena mbale, kapena mlongo wopanda mwamuna, nkuloleka kudzidetsa.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 44

Onani Ezekieli 44:25 nkhani