Ezekieli 44:7 BL92

7 popeza mwalowa nao acilendo osadulidwa m'mtima, osadulidwa m'thupi akhale m'malo anga opatulika kuwadetsa, ndiwo nyumba yanga, popereka inu mkate wanga, mafuta, ndi mwazi; ndipo munatyola pangano langa pamodzi ndi zonyansa zanu zonse.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 44

Onani Ezekieli 44:7 nkhani