13 Atero Ambuye Yehova, Malire amene mugawe nao dziko likhale colowa cao monga mwa mafuko khumi ndi awiri a Israyeli ndi awa: Yosefe akhale nao magawo awiri.
Werengani mutu wathunthu Ezekieli 47
Onani Ezekieli 47:13 nkhani