Ezekieli 8:2 BL92

2 Ndipo ndinapenya, ndipo taonani, cifaniziro ca maonekedwe a moto; kuyambira maonekedwe a m'cuuno mwace ndi kunsi kwace, moto; ndi kuyambira m'cuuno mwace ndi kumwamba kwace, monga maonekedwe a ceza, ngan citsulo cakupsa.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 8

Onani Ezekieli 8:2 nkhani