Ezekieli 8:1 BL92

1 Ndipo kunali caka cacisanu ndi cimodzi, mwezi wacisanu ndi cimodzi, tsiku lacisanu la mweziwo, pokhala ine m'nyumba mwanga, akulu a Yuda omwe analikukhala pamaso panga, dzanja la Yehova Mulungu linandigwera komweko.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 8

Onani Ezekieli 8:1 nkhani