Ezekieli 8:6 BL92

6 Ndipo anati kwa ine, Wobadwa ndi munthu iwe, uona kodi izi alikuzicita? zonyansa zazikulu nyumba ya Israyeli irikuzicita kuno, kuti ndicoke kutali kwa malo anga opatulika? Koma udzaonanso zonyansa zina zoposa.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 8

Onani Ezekieli 8:6 nkhani