Ezekieli 8:5 BL92

5 Pamenepo ananena ndi ine, Wobadwa ndi munthu iwe, kweza maso ako ku njira yoloza kumpoto. Ndipo ndinakweza maso anga ku njira yoloza kumpoto, ndipo taonani, kumpoto kwa cipata ca guwa la nsembe fano ili la nsanje polowera pace.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 8

Onani Ezekieli 8:5 nkhani