Ezekieli 9:6 BL92

6 iphanitu nkhalamba, mnyamata ndi namwali, makanda, ndi akazi; koma musayandikira munthu ali yense ali naco cizindikilo, ndipo muyambe pa malo anga opatulika, Pamenepo anayamba ndi akuluwo anali pakhomo pa nyumba.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 9

Onani Ezekieli 9:6 nkhani