Ezekieli 9:9 BL92

9 Pamenepo ananena nane, Mphulupulu ya nyumba ya Israyeli ndi Yuda ndi yaikurukuru ndithu, ndi dziko ladzala ndi mwazi, ndi mudziwo wadzala ndi kukhotetsa mirandu; pakuti ati, Yehova wataya dziko, Yehova sapenya.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 9

Onani Ezekieli 9:9 nkhani