Ezekieli 9:8 BL92

8 Ndipo kunali, alimkukantha iwo, nditatsala ine, ndinagwa nkhope yanga pansi, ndi kupfuula, ndi kuti, Kalanga ine. Ambuye Mulungu! kodi mudzaononga otsala onse a Israyeli pakutsanulira ukali wanu pa Yerusalemu?

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 9

Onani Ezekieli 9:8 nkhani