Genesis 44:2 BL92

2 Nuike cikho canga, cikho casiliva ciija, kukamwa kwa thumba la wamng'ono, pamodzi ndi ndalama za tirigu zace. Ndipo iye anacita monga mau ananena Yosefe.

Werengani mutu wathunthu Genesis 44

Onani Genesis 44:2 nkhani