Ezekieli 1:20 BL92

20 Kuli konse mzimu ukuti umuke, zinamuka komwe mzimu ukuti umuke; ndi njingazi zinanyamuka pambali pa izo; pakuti mzimu wa zamoyozo unali m'njingazo.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 1

Onani Ezekieli 1:20 nkhani