Ezekieli 20:39 BL92

39 Ndipo inu, nyumba ya Israyeli, atero Ambuye Yehova, mukani, tumikirani yense mafano ace, ndi m'tsogolo momwe, popeza simundimvera Ine; koma musaipsanso dzina langa lopatulika ndi zopereka zanu ndi mafano anu.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 20

Onani Ezekieli 20:39 nkhani