Ezekieli 32:15 BL92

15 Pakusanduliza Ine dziko la Aigupto likhale lopasuka ndi labwinja, dziko losowa zodzaza zace, pakukantha Ine onse okhala m'mwemo, pamenepo adzadziwa kuti ine ndine Yehova.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 32

Onani Ezekieli 32:15 nkhani