Ezekieli 40:7 BL92

7 Ndi cipinda ca alonda, conse nca bango limodzi m'litali mwace, ndi bango limodzi kupingasa kwace, ndi pakati pa zipinda za alonda mikono isanu, ndi ciundo ca cipata ku mbali ya ku khonde la kucipata m'katimo, bango limodzi.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 40

Onani Ezekieli 40:7 nkhani