Ezekieli 44:12 BL92

12 Popeza anawatumikira pamaso pa mafano ao, nakhala cokhumudwitsa ca mphulupulu ca nyumba ya Israyeli, cifukwa cace ndawakwezera dzanja langa, ati Ambuye Yehova; ndipo adzasenza mphulupulu yao.

Werengani mutu wathunthu Ezekieli 44

Onani Ezekieli 44:12 nkhani