Yeremiya 2:20 BL92

20 Pakuti kale lomwe ndinatyola gori lako, ndi kudula zomangira zako; ndipo unati, Sindidzakutumikirani, pakuti pa zitunda zonse zazitari, ndi patsinde pa mitengo yonse yaiwisi unawerama, ndi kucita dama.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 2

Onani Yeremiya 2:20 nkhani