Yeremiya 20:11 BL92

11 Koma Yehova ali ndi ine ngati wamphamvu ndi woopsya; cifukwa cace ondisautsa adzapunthwa, sadzandilala; adzakhala ndi manyazi ambiri, cifukwa sanacita canzeru, ngakhale ndi kunyazitsa kwamuyaya kumene sikudzaiwalika.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 20

Onani Yeremiya 20:11 nkhani