12 Cifukwa cace njira yao idzakhala kwa iwo yonga malo akuterereka m'mdima; adzacotsedwa, nadzagwa momwemo; pakuti ndidzawatengera zoipa, caka ca kulangidwa kwao, ati Yehova.
Werengani mutu wathunthu Yeremiya 23
Onani Yeremiya 23:12 nkhani