Yeremiya 23:8 BL92

8 koma, Pali Yehova, amene anakweza ndi kutsogolera mbeu za nyumba ya Israyeli kuwaturutsa m'dziko la kumpoto, ndi ku maiko onse kumene ndinawapitikitsirako, ndipo adzakhala m'dziko lao.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 23

Onani Yeremiya 23:8 nkhani