Yeremiya 24:5 BL92

5 Cifukwa Yehova, Mulungu wa Israyeli, atero, Monga nkhuyu zabwino izi, momwemo ndidzasamalira am'nsinga a Yuda, amene ndawacotsera m'malo muno kunka ku dziko la Akasidi, kuwacitira bwino.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 24

Onani Yeremiya 24:5 nkhani