Yeremiya 25:12 BL92

12 Ndipo kudzakhala, zitapita zaka makumi asanu ndi awiri, ndzidzalanga mfumu ya ku Babulo, ndi mtundu uja womwe, ati Yehova, cifukwa ca mphulupulu zao, ndi dziko la Akasidi; ndipo ndidzaliyesa mabwinja amuyaya.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 25

Onani Yeremiya 25:12 nkhani