26 ndi mafumu onse a kumpoto, a kutari ndi a kufupi, wina ndi mnzace; ndi maufumu onse a dziko lapansi, okhala pansi pano; ndi mfumu ya Sesaki adzamwa pambuyo pao.
Werengani mutu wathunthu Yeremiya 25
Onani Yeremiya 25:26 nkhani