Yeremiya 25:5 BL92

5 ndi kuti, Mubwerere tsopano nonsenu, yense kuleka njira yace yoipa, ndi zoipa za nchito zanu, ndi kukhala m'dziko limene Yehova anapatsa inu ndi makolo anu, kuyambira kale kufikira muyaya;

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 25

Onani Yeremiya 25:5 nkhani