Yeremiya 26:8 BL92

8 Ndipo panali, pamene Yeremiya anatha kunena mau onse amene Yehova anamuuza iye kuti anene kwa anthu onse, ansembe ndi aneneri ndi anthu onse anamgwira iye, ndi kuti, Udzafa ndithu.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 26

Onani Yeremiya 26:8 nkhani