Yeremiya 29:28 BL92

28 popeza watitumizira mau ku Babulo, akuti, Undende udzakhalitsa; mangani nyumba, khalani m'menemo; limani minda, idyani zipatso zao?

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 29

Onani Yeremiya 29:28 nkhani