Yeremiya 3:14 BL92

14 Bwerani, ananu obwerera, ati Yehova; pakuti Ine ndine mbuye wanu; ndipo ndidzakutengani inu mmodzi mmodzi wa pa mudzi uli wonse, ndi awiri awiri a pa banja liri lonse, ndi kukutengerani ku Ziyoni;

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 3

Onani Yeremiya 3:14 nkhani