Yeremiya 3:19 BL92

19 Koma Ine ndinati, Ndidzakuika iwe bwanji mwa ana, ndi kupatsa iwe dziko lokondweretsa, colowa cabwino ca makamu a mitundu ya anthu? ndipo ndinati mudzandicha Ine, Atate wanga; osatembenuka kuleka kunditsata Ine.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 3

Onani Yeremiya 3:19 nkhani