Yeremiya 31:19 BL92

19 Pakuti nditatembenuka, ndinalapa; nditalangizidwa, ndinamenya pa ncafu yanga; ndinakhala ndi manyazi, inde, ndinapepulidwa, cifukwa ndinasenza citonzo ca ubwana wanga.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 31

Onani Yeremiya 31:19 nkhani