Yeremiya 34:16 BL92

16 koma mwabwerera ndi kuipitsa dzina langa, ndi kubwezera m'ukapolo yense kapolo wace wamwamuna, ndi wamkazi, amene munammasula akacite zao, ndipo munawagonjetsa, akhale akapolo anu amuna ndi akazi.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 34

Onani Yeremiya 34:16 nkhani