Yeremiya 35:7 BL92

7 ndiponso musamange nyumba, musafese mbeu, musaoke mipesa, musakhale nayo; koma masiku anu onse mudzakhale m'mahema; kuti mukhale ndi moyo masiku ambiri m'dziko limene mukhalamo alendo.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 35

Onani Yeremiya 35:7 nkhani