Yeremiya 36:2 BL92

2 Tenga buku lampukutu, nulembe m'menemo mau onse ndanena kwa iwe akunenera Israyeli, ndi akunenera Yuda, ndi akunenera amitundu onse, kuyambira tsiku ndinanena kwa iwe, kuyambira masiku a Yosiya, mpaka lero.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 36

Onani Yeremiya 36:2 nkhani