Yeremiya 36:31 BL92

31 Ndipo ndidzamlanga iye ndi mbeu zace ndi atumiki ace cifukwa ca mphulupulu zao; ndipo ndidzawatengera iwo, ndi okhala m'Yerusalemu, ndi anthu a Yuda, zoipa zonse ndawanenera iwo, koma sanamvera.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 36

Onani Yeremiya 36:31 nkhani