Yeremiya 38:6 BL92

6 Ndipo anatenga Yeremiya, namponya iye m'dzenje la Malikiya mwana wace wa mfumu, limene linali m'bwalo la kaidi; ndipo anamtsitsa Yeremiya ndi zingwe, Koma m'dzenjemo munalibe madzi, koma thope; namira Yeremiya m'thopemo.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 38

Onani Yeremiya 38:6 nkhani