Yeremiya 41:8 BL92

8 Koma mwa iwo anaoneka anthu khumi amene anati kwa Ismayeli, Musatiphe ife; pakuti tiri ndi cuma cobisika m'mudzi, ca tirigu, ndi ca barele, ndi ca mafuta, ndi ca uci. Momwemo analeka, osawapha pakati pa abale ao.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 41

Onani Yeremiya 41:8 nkhani