Yeremiya 46:26 BL92

26 ndipo ndidzawapereka m'manja a iwo amene afuna moyo wao, ndi m'dzanja la Nebukadirezara mfumu ya ku Babulo, ndi m'manja a atumiki ace; pambuyo pace adzakhalamo anthu, monga masiku akale, ati Yehova.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 46

Onani Yeremiya 46:26 nkhani