Yeremiya 5:24 BL92

24 Ndipo sanena m'mtima mwao, Tiopetu Yehova Mulungu wathu wopatsa mvula yoyamba ndi yamasika, m'nyengo yace; atisungira ife masabata olamulidwa a masika.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 5

Onani Yeremiya 5:24 nkhani