Yeremiya 6:26 BL92

26 Iwe mwana wamkazi wa anthu anga, udzibveke ndi ciguduli, ndi kubvimbvinika m'phulusa; ulire maliro ngati a mwana wamwamuna wa yekha, kulira kowawa koposa; pakuti wakufunkha adzatifikira ife motidzidzimutsa.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 6

Onani Yeremiya 6:26 nkhani