Yeremiya 8:6 BL92

6 Ndinachera khutu, ndinamva koma sananena bwino; panalibe munthu amene anatembenuka kusiya zoipa zace, ndi kuti, Ndacita ciani? yense anatembenukira njira yace, monga akavalo athamangira m'nkhondo.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 8

Onani Yeremiya 8:6 nkhani