16 Mau anu anapezeka, ndipo ndinawadya; mau anu anakhala kwa ine cikondwero ndi cisangalalo ca mtima wanga; pakuti ndachedwa dzina lanu, Yehova Mulungu wa makamu.
Werengani mutu wathunthu Yeremiya 15
Onani Yeremiya 15:16 nkhani