Yeremiya 22:25 BL92

25 ndipo ndidzakupereka iwe m'dzanja la iwo amene afuna moyo wako, m'dzanja la iwo: amene uwaopa, m'dzanja la Nebukadirezara mfumu ya ku Babulo, m'dzanja la Akasidi.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 22

Onani Yeremiya 22:25 nkhani