Yeremiya 25:14 BL92

14 Pakuti mitundu yambiri ndi mafumu akuru adzayesa iwo atumiki ao; ndipo ndidzabwezera iwo monga mwa macitidwe ao, monga mwa nchito ya manja ao.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 25

Onani Yeremiya 25:14 nkhani