34 Kuwani, inu abusa, lirani, gubudukani, inu akuru a zoweta; pakuti masiku a kuphedwa kwanu akwanira ndithu, ndipo ndidzakuphwanyani inu, ndipo mudzagwa ngati cotengera cofunika.
Werengani mutu wathunthu Yeremiya 25
Onani Yeremiya 25:34 nkhani