Yeremiya 25:33 BL92

33 Ndipo akuphedwa a Yehova adzakhala tsiku lomwelo kucokera ku malekezero ena a dziko lapansi kunka ku malekezero ena a dzikolapansi, sadzaliridwa maliro, sadzasonkhanidwa, sadzaikidwa; adzakhala ngati ndowe panthaka.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 25

Onani Yeremiya 25:33 nkhani