Yeremiya 31:23 BL92

23 Atero Yehova wa makamu, Mulungu wa Israyeli, Kawirinso adzanena mau awa m'dziko la Yuda ndi m'midzi yace, pamene ndibwezanso undende wao; Yehova akudalitse iwe, wokhalamo cilungamo, iwe phiri lopatulika.

Werengani mutu wathunthu Yeremiya 31

Onani Yeremiya 31:23 nkhani